Genesis 33:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo anagula ndi ndalama zana limodzi dera la munda kumeneko anamanga hema wake, padzanja la ana ake a Hamori atate wake wa Sekemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo anagula ndi ndalama zana limodzi dera la munda kumeneko anamanga hema wake, pa dzanja la ana ake a Hamori atate wake wa Sekemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Malo amenewo adagula kwa zidzukulu za Hamori, bambo wake wa Sekemu, pa mtengo wa ndalama 100 zasiliva. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Malo amenewo anagula kwa zidzukulu za Hamori, abambo a Sekemu ndi ndalama 100 zasiliva. Onani mutuwo |