Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 33:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo Esau anabwerera tsiku lomwelo kunka ku Seiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo Esau anabwera tsiku lomwelo kunka ku Seiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Motero pa tsiku limenelo Esau adanyamuka ulendo kubwerera ku Seiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Choncho tsiku limenelo Esau anayamba ulendo wobwerera ku Seiri.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 33:16
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Yakobo anatumiza amithenga patsogolo pake kwa Esau mkulu wake, ku dziko la Seiri, kudera la ku Edomu.


Ndipo Esau anati, Ndikusiyire anthu ena amene ali ndi ine. Ndipo iye anati, Chifukwa chanji? Ndipeze ine ufulu pamaso pa mbuyanga.


Ndipo Yakobo anankabe ulendo wake ku Sukoti, namanga nyumba yake pamenepo, namanga makola a zoweta zake: chifukwa chake dzina lake la kumeneko ndi Sukoti.


Ndipo akalonga a Afilisti anamkwerera mkaziyo, nanena naye, Umkope nuone umo muchokera mphamvu yake yaikulu, ndi umo tingakhoze kumtha khama, kuti timmange kumzunza; ndipo tidzakupatsa aliyense ndalama mazana khumi ndi limodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa