Genesis 33:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo Esau anati, Ndikusiyire anthu ena amene ali ndi ine. Ndipo iye anati, Chifukwa chanji? Ndipeze ine ufulu pamaso pa mbuyanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo Esau anati, Ndikusiyire anthu ena amene ali ndi ine. Ndipo iye anati, Chifukwa chanji? Ndipeze ine ufulu pamaso pa mbuyanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Apo Esau adati, “Tsono undilole kuti ndikusiyire anthu anga enaŵa.” Koma Yakobe adati, “Iyai mbuyanga, zimenezo sizifunika kwenikweni, ndingofuna kukukondwetsani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Esau anati, “Ndiye bwanji ndikusiyireko ena mwa anthu anga.” Koma Yakobo anati, “Koma muchitiranji zimenezi? Chachikulu nʼkuti mwandilandira bwino, mbuye wanga.” Onani mutuwo |