Genesis 32:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo anatsala Yakobo yekha; ndipo analimbana naye munthu kufikira mbandakucha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo anatsala Yakobo yekha; ndipo analimbana naye munthu kufikira mbandakucha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Iye adangotsala yekha. Tsono kudadza munthu wina amene adalimbana naye mpaka m'matandakucha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Tsono Yakobo anatsala yekha. Tsono munthu wina anadzalimbana naye mpaka mʼmbandakucha. Onani mutuwo |