Genesis 32:14 - Buku Lopatulika14 mbuzi zazikazi mazana awiri, atonde makumi awiri, nkhosa zazikazi mazana awiri, ndi zazimuna makumi awiri, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 mbuzi zazikazi mazana awiri, atonde makumi awiri, nkhosa zazikazi mazana awiri, ndi zazimuna makumi awiri, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 mbuzi zazikazi 200 ndi atonde makumi aŵiri, nkhosa zazikazi 200 ndi zamphongo makumi aŵiri, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Anasankhula mbuzi zazikazi 200 ndi atonde makumi awiri, nkhosa zazikazi 200 ndi nkhosa zazimuna makumi awiri, Onani mutuwo |