Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 32:15 - Buku Lopatulika

15 ngamira zamkaka makumi atatu ndi ana ao, ng'ombe zazikazi makumi anai, zazimuna khumi, abulu aakazi makumi awiri ndi ana khumi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 ngamira zamkaka makumi atatu ndi ana ao, ng'ombe zazikazi makumi anai, zazimuna khumi, abulu akazi makumi awiri ndi ana khumi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 ngamira zamkaka makumi atatu pamodzi ndi ana ake, ng'ombe zazikazi makumi anai, ndi zazimuna khumi, ndi abulu aakazi makumi aŵiri ndi amphongo khumi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 ngamira za mkaka 30 ndi ana awo, ngʼombe zazikazi 40 ndi zazimuna khumi, ndipo abulu aakazi makumi awiri ndi abulu aamuna khumi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 32:15
2 Mawu Ofanana  

mbuzi zazikazi mazana awiri, atonde makumi awiri, nkhosa zazikazi mazana awiri, ndi zazimuna makumi awiri,


Ndipo anazipereka zimenezo m'manja a anyamata ake, gulu pa lokha gulu pa lokha: ndipo anati kwa anyamata ake, Taolokani patsogolo panga, tachitani danga pakati pa magulu, lina ndi lina.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa