Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 31:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo inu mudziwa kuti ndi mphamvu zanga zonse ndatumikira atate wanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo inu mudziwa kuti ndi mphamvu zanga zonse ndatumikira atate wanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Nonse aŵirinu mukudziŵa bwino kuti ndidagwira ntchito kwa bambo wanu ndi mphamvu zanga zonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Inu mukudziwa kuti ndagwirira ntchito abambo anu ndi mphamvu zanga zonse,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 31:6
8 Mawu Ofanana  

Undipatse ine akazi anga ndi ana anga chifukwa cha iwowa ndakutumikira iwe, ndimuke: chifukwa udziwa iwe ntchito imene ndinakugwirira iwe.


Ndipo iye anati kwa Labani, Udziwa iwe chomwe ndakutumikira iwe ndi chomwe zachita zoweta zako ndi ine.


Ndipo atate wanu wandinyenga ine, nasinthanitsa malipiro anga kakhumi; koma Mulungu sanamlole iye andichitire ine choipa.


Anyamata inu, gonjerani ambuye anu ndi kuopa konse, osati abwino ndi aulere okha, komanso aukali.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa