Genesis 31:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo atate wanu wandinyenga ine, nasinthanitsa malipiro anga kakhumi; koma Mulungu sanamlole iye andichitire ine choipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo atate wanu wandinyenga ine, nasinthanitsa malipiro anga kakhumi; koma Mulungu sanamlole iye andichitire ine choipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Komabe iye wandipusitsa, ndipo malipiro anga waasinthasintha kakhumi konse. Koma Mulungu sadamlole kuti andichite choipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 chonsecho abambo anu akhala akundinyenga posintha malipiro anga kakhumi konse. Komabe Mulungu sanalole kuti andichitire choyipa Onani mutuwo |