Genesis 31:5 - Buku Lopatulika5 ndipo anati kwa iwo, Ndiona ine nkhope ya atate wanu kuti siindionekere ine monga kale; koma Mulungu wa atate wanga anali ndi ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndipo anati kwa iwo, Ndiona ine nkhope ya atate wanu kuti siindionekera ine monga kale; koma Mulungu wa atate wanga anali ndi ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Atafikako, iye adaŵauza kuti, “Ndaona kuti bambo wanu tsopano sakundipenya ndi maso abwino ngati kale. Koma Mulungu wa atate anga wakhala nane. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Iye anawawuza kuti, “Abambo anu sakundionetsanso nkhope yabwino monga kale, koma Mulungu wa makolo anga wakhala ali nane. Onani mutuwo |