Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 31:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo Yakobo anatumiza naitana Rakele ndi Leya adze kubusa ku zoweta zake,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo Yakobo anatumiza naitana Rakele ndi Leya adze kubusa ku zoweta zake,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Tsono Yakobe adatumiza mau kwa Rakele ndi kwa Leya kuti akakumane naye kubusa kumene kunali zoŵeta zake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Choncho Yakobo anatumiza mawu kukayitana Rakele ndi Leya kuti abwere ku busa kumene ankaweta ziweto zake.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 31:4
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Labani anali ndi ana aakazi awiri, dzina la wamkulu ndi Leya, dzina la wamng'ono ndi Rakele.


Ndipo Yehova anati kwa Yakobo, Bwera ku dziko la atate wako, ndi kwa abale ako, ndipo ndidzakhala ndi iwe.


ndipo anati kwa iwo, Ndiona ine nkhope ya atate wanu kuti siindionekere ine monga kale; koma Mulungu wa atate wanga anali ndi ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa