Genesis 31:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Yehova anati kwa Yakobo, Bwera ku dziko la atate wako, ndi kwa abale ako, ndipo ndidzakhala ndi iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Yehova anati kwa Yakobo, Bwera ku dziko la atate wako, ndi kwa abale ako, ndipo ndidzakhala ndi iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono Chauta adamuuza kuti, “Bwerera ku dziko la atate ako ndi kwa abale ako. Ine ndidzakhala nawe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pamenepo Yehova anati kwa Yakobo, “Bwerera ku dziko la makolo ako ndi kwa abale ako, ndipo Ine ndidzakhala nawe.” Onani mutuwo |