Genesis 31:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Yakobo anaona nkhope ya Labani, taonani, siinamuonekere iye monga kale. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Yakobo anaona nkhope ya Labani, taonani, siinamuonekera iye monga kale. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Yakobe adazindikiranso kuti Labani sankamuwonetsa nkhope yabwino ngati kale. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Choncho Yakobo anaona kuti Labani sankamuonetsanso nkhope yabwino monga kale. Onani mutuwo |