Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 31:52 - Buku Lopatulika

52 Muluwu ndiwo mboni, choimiritsachi ndicho mboni, kuti ine sindidzapitirira pa muluwu kunka kwa iwe, ndipo iwe sudzapitirira pa muluwu ndi pa choimiritsachi kudza kwa ine kuti tichitirane zoipa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

52 Muluwu ndiwo mboni, choimiritsachi ndicho mboni, kuti ine sindidzapitirira pa muluwu kunka kwa iwe, ndipo iwe sudzapitirira pa muluwu ndi pa choimiritsachi kudza kwa ine kuti tichitirane zoipa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

52 Mulu umenewu pamodzi ndi mwala wachikumbutsowu, zonsezi ndi mboni. Ine sindidzapyola mulu umenewu kuti ndilimbane nawe. Iwenso usadzapyole muluwu kuti ulimbane ndi ine.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

52 Mulu wa miyala uwu ndi chipilalachi ndi mboni. Ine sindidzadutsa mulu wa miyalawu kudzalimbana ndi iwe. Iwenso usadzadutse mulu wa miyalawu kudzalimbana nane.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 31:52
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Labani anati, Muluwu ndiwo mboni pakati pa ine ndi iwe lero. Chifukwa chake anatcha dzina lake, Galedi;


Ndipo Labani anati kwa Yakobo. Taona muluwu, taona choimiritsachi, ndachiimiritsa pakati pathu.


Mulungu wa Abrahamu ndi Mulungu wa Nahori, Mulungu wa atate wao aweruze pa ife. Ndipo Yakobo analumbirira pa Kuopsa kwa atate wake Isaki.


koma lidzakhala mboni pakati pa ife ndi inu, ndi pakati pa mibadwo yathu ya m'tsogolo, kuti tikachita ntchito ya Yehova pamaso pake ndi nsembe zathu zopsereza, ndi zophera, ndi zoyamika; kuti ana anu asanene ndi ana athu m'tsogolomo, Mulibe gawo ndi Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa