Genesis 31:53 - Buku Lopatulika53 Mulungu wa Abrahamu ndi Mulungu wa Nahori, Mulungu wa atate wao aweruze pa ife. Ndipo Yakobo analumbirira pa Kuopsa kwa atate wake Isaki. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201453 Mulungu wa Abrahamu ndi Mulungu wa Nahori, Mulungu wa atate wao aweruze pa ife. Ndipo Yakobo analumbirira pa Kuopsa kwa atate wake Isaki. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa53 Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Nahori, Mulungu wa atate ao, ndiye adzatiweruze ife aŵiri.” Motero Yakobe adalumbira m'dzina la Mulungu amene Isaki bambo wake ankamuwopa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero53 Mulungu wa Abrahamu ndi Mulungu wa Nahori ndiye adzatiweruze.” Choncho Yakobo analumbira mʼdzina la Mulungu amene Isake, abambo ake ankamuopa. Onani mutuwo |