Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 31:51 - Buku Lopatulika

51 Ndipo Labani anati kwa Yakobo. Taona muluwu, taona choimiritsachi, ndachiimiritsa pakati pathu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

51 Ndipo Labani anati kwa Yakobo. Taona muluwu, taona choimiritsachi, ndachiimiritsa pakati pathu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

51 Tsono Labani adauza Yakobe kuti, “Pano pali miyala imene ndaunjika pakati pathu, ndipo pompano pali mwala wachikumbutso.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

51 Labani anatinso kwa Yakobo, “Taona pano pali miyala ndi chipilala chimene ndayimika pakati pa iwe ndi ine.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 31:51
2 Mawu Ofanana  

Ukasautsa ana anga aakazi, kapena ukatenga akazi kuonjezera pa ana anga, palibe munthu mmodzi ali nafe; taonani, Mulungu ndiye mboni yanga ndi yako.


Muluwu ndiwo mboni, choimiritsachi ndicho mboni, kuti ine sindidzapitirira pa muluwu kunka kwa iwe, ndipo iwe sudzapitirira pa muluwu ndi pa choimiritsachi kudza kwa ine kuti tichitirane zoipa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa