Genesis 31:44 - Buku Lopatulika44 Tsopano tiyeni tipangane pangano, ine ndi iwe; likhale mboni pakati pa ine ndi iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 Tsopano tiyeni tipangane pangano, ine ndi iwe; likhale mboni pakati pa ine ndi iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 Chabwino, tiye tichite chipangano, chikhale mboni pakati pa ine ndi iwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 Tsono, tiye tichite pangano pakati pa iwe ndi ine, ndipo likhale mboni pakati pathu.” Onani mutuwo |