Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 31:45 - Buku Lopatulika

45 Ndipo Yakobo anatenga mwala, nauimiritsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

45 Ndipo Yakobo anatenga mwala, nauimiritsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

45 Yakobe adaimiritsa mwala.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

45 Choncho Yakobo anayimiritsa mwala ngati chipilala.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 31:45
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yakobo anati kwa abale ake, Sonkhanitsani miyala; ndipo anasonkhanitsa miyala nakundika mulu: ndipo anadya pamulupo.


Ndipo Yakobo anaimiritsa mwala pamalo pamene ananena ndi iye, choimiritsa chamwala: ndipo anathira pamenepo nsembe yothira, nathirapo mafuta.


Ndipo Yoswa analembera mau awa m'buku la chilamulo cha Mulungu; natenga mwala waukulu, nauimitsa apo patsinde pa thundu wokhala pamalo opatulika a Yehova.


Ndipo Yoswa anati kwa anthu onse, Taonani, mwala uwu udzakhala mboni yotitsutsa; pakuti udamva mau onse a Yehova amene ananena kwa ife; ndipo udzakhala mboni yotsutsa inu, mungakanize Mulungu wanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa