Genesis 31:45 - Buku Lopatulika45 Ndipo Yakobo anatenga mwala, nauimiritsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Ndipo Yakobo anatenga mwala, nauimiritsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 Yakobe adaimiritsa mwala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 Choncho Yakobo anayimiritsa mwala ngati chipilala. Onani mutuwo |