Genesis 30:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo Biliha mdzakazi wake wa Rakele anatenganso pakati, nambalira Yakobo mwana wamwamuna wachiwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo Biliha mdzakazi wake wa Rakele anatenganso pakati, nambalira Yakobo mwana wamwamuna wachiwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Biliha mdzakazi wa Rakele adatenganso pathupi namubaliranso Yakobe mwana wamwamuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Biliha, wantchito wa Rakele, anatenganso pathupi nabalira Yakobo mwana wa mwamuna wachiwiri. Onani mutuwo |