Genesis 30:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Biliha anatenga pakati, nambalira Yakobo mwana wamwamuna. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Biliha anatenga pakati, nambalira Yakobo mwana wamwamuna. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Biliha adatenga pathupi namubalira Yakobe mwana wamwamuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 ndipo Bilihayo anatenga pathupi namubalira Yakobo mwana wamwamuna. Onani mutuwo |