Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 30:36 - Buku Lopatulika

36 Ndipo iye yekha anatalikitsana ndi Yakobo ulendo wa masiku atatu: ndipo Yakobo anadyetsa ziweto zina za Labani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Ndipo iye yekha anatalikitsana ndi Yakobo ulendo wa masiku atatu: ndipo Yakobo anadyetsa ziweto zina za Labani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Atatero adasiyana naye Yakobe uja nayenda mtunda wa masiku atatu. M'menemo nkuti Yakobeyo akuŵeta zoŵeta zina za Labani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Kenaka Labani anayenda mtunda wa masiku atatu kutalikirana ndi Yakobo koma Yakobo anapitiriza kuweta nkhosa zina zonse za Labani.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 30:36
3 Mawu Ofanana  

Tsiku lomwelo Labani anachotsa atonde amene anali amipyololomipyololo ndi amathothomathotho, ndi mbuzi zazikazi zinali zamawangamawanga ndi zamathothomathotho zonse zinali zoyera pang'ono, ndi zakuda zonse za nkhosa, napatsa m'dzanja la ana ake aamuna.


Ndipo Yakobo anatenga nthyole za mtengo wauwisi wa libne, ndi za mtengo wakatungurume, ndi za mtengo waarimoni, nakupula m'menemo mizere yoyera, naonetsa moyera mwa m'nthyolemo.


Tsiku lachitatu anamuuza Labani kuti Yakobo wathawa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa