Genesis 30:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo Yakobo anatenga nthyole za mtengo wauwisi wa libne, ndi za mtengo wakatungurume, ndi za mtengo waarimoni, nakupula m'menemo mizere yoyera, naonetsa moyera mwa m'nthyolemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo Yakobo anatenga nthyole za mtengo wowisi walibne, ndi za mtengo wakatungurume, ndi za mtengo waarimoni, nakupula m'menemo mizere yoyera, naonetsa moyera mwa m'nthyolemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Tsono Yakobe adatenga nthambi zaziŵisi za mitengo ya mitundu itatu yakudzikolo, nazikungunula makungwa, kotero kuti nthambizo zinkaoneka za mipyololo yoyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Tsono Yakobo anatenga nthambi zaziwisi za mitengo ya mkundi, alimoni ndi puleni nazisenda kuchotsa makungwa ake mpaka mtengo woyera wamʼkati kuonekera. Onani mutuwo |