Genesis 30:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo Labani anati, Taona, kukhale monga mau ako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo Labani anati, Taona, kukhale monga mau ako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Labani adavomera, adati, “Chabwino. Tichite monga waneneramo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Labani anati, “Ndavomera, zikhale monga mmene wayankhuliramu.” Onani mutuwo |