Genesis 30:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo panali pamene Rakele anabala Yosefe, Yakobo anati kwa Labani, Undisudzule ine ndinke kwathu ku dziko langa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo panali pamene Rakele anabala Yosefe, Yakobo anati kwa Labani, Undisudzule ine ndinke kwathu ku dziko langa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Atabadwa Yosefe, Yakobe adauza Labani kuti, “Mundilole ndizibwerera kwathu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Rakele atabereka Yosefe, Yakobo anati kwa Labani, “Ndimasuleni kuti ndizipita ku dziko la kwathu. Onani mutuwo |