Genesis 30:24 - Buku Lopatulika24 namutcha dzina lake Yosefe; ndipo anati, Yehova anandionjezera ine mwana wamwamuna wina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 namutcha dzina lake Yosefe; ndipo anati, Yehova anandionjezera ine mwana wamwamuna wina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Motero mwanayo adamutcha Yosefe, nanena kuti, “Mulungu andipatse wina mwana.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Iye anamutcha mwanayo Yosefe, ndipo anati, “Mulungu andipatsenso mwana wina.” Onani mutuwo |