Genesis 30:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo anatenga pakati, nabala mwana wamwamuna, nati, Mulungu wachotsa manyazi anga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo anatenga pakati, nabala mwana wamwamuna, nati, Mulungu wachotsa manyazi anga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Iyenso adatenga pathupi, nabala mwana wamwamuna. Ndipo adati, “Mulungu wandichotsa manyazi a uchumba wanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Rakele anatenga pathupi nabala mwana wamwamuna ndipo anati, “Mulungu wandichotsera manyazi anga.” Onani mutuwo |