Genesis 30:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo Mulungu anakumbukira Rakele, ndipo Mulungu anamvera iye, natsegula m'mimba mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo Mulungu anakumbukira Rakele, ndipo Mulungu anamvera iye, natsegula m'mimba mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Tsono Mulungu adakumbukira Rakele, namva pemphero lake, nkulola kuti abale ana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Kenaka, Mulungu anakumbukira Rakele namva pemphero lake ndi kulola kuti akhale ndi mwana. Onani mutuwo |