Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 30:21 - Buku Lopatulika

21 Pambuyo pake ndipo anabala mwana wamkazi, namutcha dzina lake Dina.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Pambuyo pake ndipo anabala mwana wamkazi, namutcha dzina lake Dina.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Pambuyo pake adabala mwana wamkazi, namutcha Dina.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Patapita nthawi Leya anabereka mwana wamkazi ndipo anamutcha Dina.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 30:21
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Leya anati, Mulungu anandipatsa ine mphatso yabwino; tsopano mwamuna wanga adzakhala ndi ine, chifukwa ndambalira iye ana aamuna asanu ndi mmodzi; ndipo anamutcha dzina lake Zebuloni.


Ndipo Mulungu anakumbukira Rakele, ndipo Mulungu anamvera iye, natsegula m'mimba mwake.


Ndipo anapha Hamori ndi Sekemu mwana wake ndi lupanga, natulutsa Dina m'nyumba ya Sekemu nachoka naye.


Amenewo ndi ana aamuna a Leya, amene anambalira Yakobo ku Padanaramu, pamodzi ndi mwana wamkazi wake Dina; ana aamuna ndi aakazi onse ndiwo anthu makumi atatu kudza atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa