Genesis 30:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Leya anati, Ndakondwa ine! Chifukwa kuti ana aakazi adzanditcha ine wokondwa: ndipo anamutcha dzina lake Asere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Leya anati, Ndakondwa ine! Chifukwa kuti ana akazi adzanditcha ine wokondwa: ndipo anamutcha dzina lake Asere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Apo Leya adati, “Ndakondwa! Ndipo akazi adzanditchula wamwai.” Motero mwanayo adamutcha Asere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pamenepo Leya anati, “Ndakondwa bwanji! Amayi adzanditcha ine wokondwa.” Choncho anamutcha Aseri. Onani mutuwo |