Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 30:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo Zilipa mdzakazi wa Leya anambalira Yakobo mwana wamwamuna wachiwiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo Zilipa mdzakazi wa Leya anambalira Yakobo mwana wamwamuna wachiwiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Zilipa mdzakazi wa Leyayo adamubaliranso Yakobe mwana wamwamuna wachiŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Zilipa, wantchito wa Leya anamubalira Yakobo mwana wa mwamuna wachiwiri.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 30:12
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Leya anati, Wamwai ine! Ndipo anamutcha dzina lake Gadi.


Ndipo Leya anati, Ndakondwa ine! Chifukwa kuti ana aakazi adzanditcha ine wokondwa: ndipo anamutcha dzina lake Asere.


Ndi m'malire a Dani, kuyambira mbali ya kum'mawa kufikira mbali ya kumadzulo; Asere, limodzi.


A ana a Asere, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa