Genesis 30:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Leya anati, Wamwai ine! Ndipo anamutcha dzina lake Gadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Leya anati, Wamwai ine! Ndipo anamutcha dzina lake Gadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono Leya adati, “Ndachita mwai.” Motero mwanayo adamutcha Gadi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Pamenepo Leya anati, “Mwayi wangawo!” Choncho anamutcha Gadi. Onani mutuwo |