Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 30:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo Zilipa mdzakazi wake wa Leya anambalira Yakobo mwana wamwamuna.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo Zilipa mdzakazi wake wa Leya anambalira Yakobo mwana wamwamuna.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Ndipo Zilipa adabala mwana wamwamuna.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Zilipa, wantchito wa Leya, anaberekera Yakobo mwana wamwamuna.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 30:10
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Leya anati, Wamwai ine! Ndipo anamutcha dzina lake Gadi.


Pamene Leya anaona kuti analeka kubala, anatenga Zilipa mdzakazi wake, nampatsa iye kwa Yakobo kuti akhale mkazi wake.


ndipo ana aamuna a Zilipa mdzakazi wake wa Leya: ndiwo Gadi ndi Asere: amenewo ndi ana aamuna a Yakobo amene anabala iye mu Padanaramu.


Ndi kumalire a Zebuloni, kuyambira kumbali ya kum'mawa kufikira mbali ya kumadzulo; Gadi, limodzi.


A ana a Gadi, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


Koma ana a Rubeni ndi ana Gadi anali nazo zoweta zambirimbiri; ndipo anapenyerera dziko la Yazere, ndi dziko la Giliyadi, ndipo taonani, malowo ndiwo malo a zoweta.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa