Genesis 3:3 - Buku Lopatulika3 Koma zipatso za mtengo umene uli m'kati mwa munda, Mulungu anati, Musadye umenewo, musakhudze umenewo, mungadzafe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma zipatso za mtengo umene uli m'kati mwa munda, Mulungu anati, Musadye umenewo, musakhudze umenewo, mungadzafe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 kupatula wokhawo umene uli pakati pake. Mulungu adanena kuti tisadye zipatso za mtengo umenewo, ngakhale kuzikhudza, chifukwa choti tikadzangotero, tidzafa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 koma Mulungu anati, ‘Musadye zipatso za mu mtengo umene uli pakati pa munda, ndipo musadzawukhudze kuti mungadzafe.’ ” Onani mutuwo |