Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 3:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 koma Mulungu anati, ‘Musadye zipatso za mu mtengo umene uli pakati pa munda, ndipo musadzawukhudze kuti mungadzafe.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 Koma zipatso za mtengo umene uli m'kati mwa munda, Mulungu anati, Musadye umenewo, musakhudze umenewo, mungadzafe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Koma zipatso za mtengo umene uli m'kati mwa munda, Mulungu anati, Musadye umenewo, musakhudze umenewo, mungadzafe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 kupatula wokhawo umene uli pakati pake. Mulungu adanena kuti tisadye zipatso za mtengo umenewo, ngakhale kuzikhudza, chifukwa choti tikadzangotero, tidzafa.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 3:3
12 Mawu Ofanana  

Tsono kumaloto komweko Mulungu anati kwa iye, “Inde ndikudziwa kuti wachita izi moona mtima, ndipo Ine sindinafune kuti undichimwire. Nʼchifukwa chake sindinakulole kuti umukhudze.


Mkaziyo anati kwa njokayo, “Tikhoza kudya zipatso za mʼmitengo ya mʼmundawu,


“Ndithudi simudzafa,” inatero njokayo kwa mkaziyo.


“Musakhudze odzozedwa anga; musawachitire choyipa aneneri anga.”


Koma tatambasulani dzanja lanu ndi kukantha zonse ali nazo ndipo iyeyo adzakutukwanani ndithu pamaso panu.”


“Mvereni chisoni, inu abwenzi anga, mvereni chisoni, pakuti dzanja la Mulungu landikantha.


Koma tatambasulani dzanja lanu ndi kuwononga thupi lake, ndipo iyeyo adzakutukwanani ndithu pamaso panu.”


Tsopano pa zinthu zomwe munandilembera nʼkwabwino kuti munthu asakwatire.


Nʼchifukwa chake “Tulukani pakati pawo ndi kudzipatula, akutero Ambuye. Musakhudze chodetsedwa chilichonse, ndipo ndidzakulandirani.”


“Usagwire chakuti,” “Usalawe chakuti,” “Usakhudze chakuti?”


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa