Genesis 29:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo anati kwa iwo, Kodi mumdziwa Labani mwana wake wa Nahori? Nati, Timdziwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo anati kwa iwo, Kodi mumdziwa Labani mwana wake wa Nahori? Nati, Timdziwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Yakobe adafunsanso kuti, “Kodi Labani mwana wa Nahori mumamdziŵa?” Iwowo adayankha kuti, “Ee, timamdziŵa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Iye anawafunsanso kuti, “Kodi Labani, mdzukulu wa Nahori mukumudziwa?” Iwo anayankha, “Inde tikumudziwa?” Onani mutuwo |