Genesis 29:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo anati Yakobo kwa iwo, Abale anga, ndinu a kuti inu? Nati, Ndife a ku Harani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo anati Yakobo kwa iwo, Abale anga, ndinu a kuti inu? Nati, Ndife a ku Harani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Yakobe adaŵafunsa abusawo kuti, “Kodi abale anga mukuchokera kuti?” Iwowo adayankha kuti, “Tikuchokera ku Harani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Yakobo anafunsa abusawo kuti, “Abale anga, mwachokera kuti?” Iwo anayankha, “Tachokera ku Harani.” Onani mutuwo |