Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 29:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo panali pamene Yakobo anaona Rakele, mwana wamkazi wa Labani, mlongo wake wa amake, ndi nkhosa za Labani mlongo wake wa amake, Yakobo anayandikira nagubuduza kuuchotsa mwala pachitsime, nazimwetsa zoweta za Labani, mlongo wake wa amake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo panali pamene Yakobo anaona Rakele, mwana wamkazi wa Labani, mlongo wake wa amake, ndi nkhosa za Labani mlongo wake wa amake, Yakobo anayandikira nagubuduza kuuchotsa mwala pachitsime, nazimwetsa zoweta za Labani, mlongo wake wa amake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Yakobe ataona Rakele ali ndi nkhosa za bambo wake Labani, adapita kuchitsimeko, nakunkhuniza mwalawo, nkuzimwetsa madzi nkhosa za Labanizo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Yakobo ataona Rakele mwana wa Labani, mlongo wa amayi ake, ali ndi nkhosa za Labani, anapita nawugudubuza mwala uja nazimwetsa madzi nkhosa za amalume akezo.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 29:10
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Yakobo anampsompsona Rakele nakweza mau ake, nalira.


Ali chilankhulire nao, anafika Rakele ndi nkhosa za atate wake, chifukwa anaziweta.


Ndipo wansembe wa Midiyani anali nao ana aakazi asanu ndi awiri, amene anadza kudzatunga madzi; ndipo anadzaza mimwero kuti amwetse gulu la atate wao.


Pamenepo anadza abusa nawapirikitsa; koma Mose anauka nawathandiza, namwetsa gulu lao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa