Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 29:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo Yakobo anampsompsona Rakele nakweza mau ake, nalira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo Yakobo anampsompsona Rakele nakweza mau ake, nalira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Tsono Yakobe adamumpsompsona Rakeleyo, nalira mokweza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Kenaka Yakobo anapsompsona Rakele nayamba kulira mokweza.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 29:11
10 Mawu Ofanana  

Ndipo Isaki atate wake anati kwa iye, Senderatu, undimpsompsone mwana wanga.


Ndipo panali pamene Yakobo anaona Rakele, mwana wamkazi wa Labani, mlongo wake wa amake, ndi nkhosa za Labani mlongo wake wa amake, Yakobo anayandikira nagubuduza kuuchotsa mwala pachitsime, nazimwetsa zoweta za Labani, mlongo wake wa amake.


Ndipo panali pamene Labani anamva mbiri ya Yakobo mwana wa mlongo wake, iye anathamangira kukakomana naye namfungatira, nampsompsona, namlowetsa m'nyumba mwake. Ndipo iye anamfotokozera Labani zinthu zonsezo.


Ndipo Esau anathamangira kukomana naye namfungatira, nagwa pankhope pake, nampsompsona; ndipo analira iwo.


Yosefe ndipo anafulumira, chifukwa mtima wake unakhumbitsa mphwake, ndipo anafuna polirira; nalowa m'chipinda chake naliramo.


Ndipo analira momveka, ndipo anamva Aejipito, ndipo anamva a m'nyumba ya Farao.


Ndipo Mose anatuluka kukakomana ndi mpongozi wake, nawerama, nampsompsona; nafunsana ali bwanji, nalowa m'hema.


Ndipo Yehova ananena ndi Aroni, Muka kuchipululu kukakomana ndi Mose. Ndipo anamuka, nakomana naye paphiri la Mulungu, nampsompsona.


Mupatsane moni wina ndi mnzake ndi kupsompsonana kopatulika. Mipingo yonse ya Khristu ikupatsani moni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa