Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 29:9 - Buku Lopatulika

9 Ali chilankhulire nao, anafika Rakele ndi nkhosa za atate wake, chifukwa anaziweta.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ali chilankhulire nao, anafika Rakele ndi nkhosa za atate wake, chifukwa anaziweta.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Yakobe akulankhulabe ndi iwowo, Rakele adafika ndi nkhosa za atate ake. Iyeyo ndiye ankaŵeta nkhosazo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ali chiyankhulire nawo, Rakele anafika ndi nkhosa za abambo ake popeza ndiye amene ankaweta nkhosazo.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 29:9
7 Mawu Ofanana  

Ndipo panali, asanathe kunena, taonani, anatuluka Rebeka, amene anambala Betuele, mwana wamwamuna wa Milika, mkazi wa Nahori mphwake wa Abrahamu, ndi mtsuko wake paphewa pake.


Ndipo panali pamene Yakobo anaona Rakele, mwana wamkazi wa Labani, mlongo wake wa amake, ndi nkhosa za Labani mlongo wake wa amake, Yakobo anayandikira nagubuduza kuuchotsa mwala pachitsime, nazimwetsa zoweta za Labani, mlongo wake wa amake.


Ndipo anati, Sitingathe, koma zitasonkhana ziweto zonse, ndipo atagubuduza mwala kuuchotsa pakamwa pa chitsime ndiko; pamenepo ndipo tizimwetsa nkhosa.


Ndipo Mose anavomera kukhala naye munthuyo; ndipo anampatsa Mose mwana wake wamkazi Zipora.


Pakukwera kumzindako anapeza anthu aakazi alikutuluka kuti akatunge madzi, nanena nao, Mlauliyo alipo kodi?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa