Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 27:32 - Buku Lopatulika

32 Ndipo Isaki atate wake anati kwa iye, Ndiwe yani? Ndipo iye anati, Ndine mwana wanu woyamba Esau.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Ndipo Isaki atate wake anati kwa iye, Ndiwe yani? Ndipo iye anati, Ndine mwana wanu woyamba Esau.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Isaki adamufunsa kuti, “Kodi iwenso ndiwe yani?” Iye adayankha kuti, “Ndine mwana wanu wamkulu Esau.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Abambo ake, Isake, anamufunsa kuti, “Ndiwe yani?” Iye anayankha, “Ndine mwana wanu woyamba Esau.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 27:32
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anati Yakobo, Undilumbirire ine lero lomwe, ndipo analumbirira iye; nagulana ndi Yakobo ukulu wake.


Ndipo Yakobo anampatsa Esau mkate ndi mphodza zophika; ndipo iye anadya, namwa, nanyamuka, napita: chomwecho Esau ananyoza ukulu wake.


Ndipo iye analowa kwa atate wake, nati, Atate wanga; iye anati, Ndine pano; ndani iwe mwana wanga?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa