Genesis 26:35 - Buku Lopatulika35 Ndipo iwo anapweteka mtima wa Isaki ndi wa Rebeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 ndipo iwo anapweteka mtima wa Isaki ndi wa Rebeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Onseŵa adapezetsa Isaki ndi Rebeka mavuto aakulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Akazi awiriwa anasandutsa Isake ndi Rebeka kukhala ndi moyo wa madandawulo nthawi zonse. Onani mutuwo |