Genesis 26:33 - Buku Lopatulika33 Ndipo anatcha dzina lake Siba, chifukwa chake dzina la mzindawo ndi Beereseba kufikira lero lino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Ndipo anatcha dzina lake Siba, chifukwa chake dzina la mudziwo ndi Beereseba kufikira lero lino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Isaki adachitcha Siba. Nchifukwa chake mzindawo umatchedwa Beereseba mpaka lero lino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Iye chitsimecho anachitcha Pangano. Nʼchifukwa chake mzindawu umatchedwa Beeriseba mpaka lero. Onani mutuwo |