Genesis 26:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Yehova anamuonekera iye nati, Usatsikire ku Ejipito, khala m'dziko m'mene ndidzakuuza iwe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Yehova anamuonekera iye nati, Usatsikire ku Ejipito, khala m'dziko m'mene ndidzakuuza iwe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono Chauta adaonekera Isaki namuuza kuti, “Usapite ku Ejipito, koma ukhale m'dziko limene ndidzakuuza kuti ukhalemo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yehova anadza kwa Isake nati, “Usapite ku Igupto; koma ukhale mʼdziko limene ndidzakuwuza kuti ukakhalemo. Onani mutuwo |