Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 26:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo Abimeleki anati kwa Isaki, Uchoke kwa ife chifukwa kuti iwe uli wamphamvu wopambana ife.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo Abimeleki anati kwa Isaki, Uchoke kwa ife chifukwa kuti iwe uli wamphamvu wopambana ife.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Tsono Abimeleki adauza Isaki kuti, “Muchoke kuno. Inu ndinu amphamvu kupambana ife.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Ndipo Abimeleki anati kwa Isake, “Muchoke pakati pathu chifukwa mwasanduka wamphamvu kuposa ife.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 26:16
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Isaki anachoka kumeneko, namanga hema wake m'chigwa cha Gerari, nakhala kumeneko.


Ndipo ananena ndi anthu ake, Taonani, anthu, ndiwo ana a Israele, achuluka, natiposa mphamvu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa