Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 26:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo zitsime zonse anakumba anyamata a atate wake, Abrahamuyo akali moyo, Afilisti anazitseka, nazikwirira ndi dothi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo zitsime zonse anakumba anyamata a atate wake, Abrahamuyo akali moyo, Afilisti anazitseka, nazikwirira ndi dothi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 (Anthuwo anali atakwirira zitsime zonse zimene antchito a bambo wake Abrahamu adaakumba, Abrahamuyo adakali ndi moyo.)

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Nthawi iyi nʼkuti Afilisti atakwirira ndi dothi zitsime zonse zimene antchito abambo ake Abrahamu anakumba mu nthawi ya abambo akewo.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 26:15
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anamdzudzula Abimeleki chifukwa cha chitsime cha madzi, anyamata ake a Abimeleki anachilanda.


Ndipo anati, Anaankhosa aakazi asanu ndi awiriwa uwalandire padzanja langa, kuti akhale mboni zanga, kuti ndakumba ine chitsime chimenechi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa