Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 26:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo Isaki anachoka kumeneko, namanga hema wake m'chigwa cha Gerari, nakhala kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo Isaki anachoka kumeneko, namanga hema wake m'chigwa cha Gerari, nakhala kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Motero Isaki adachoka nakamanga mahema m'chigwa cha Gerari nakhazikikako.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Choncho Isake anachokako kumeneko nakakhala ku chigwa cha Gerari kumene anakhazikikako.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 26:17
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Abimeleki anati kwa Isaki, Uchoke kwa ife chifukwa kuti iwe uli wamphamvu wopambana ife.


Ndipo Isaki anafukulanso zitsime za madzi, anazikumba masiku a Abrahamu atate wake; chifukwa kuti Afilisti anazitseka atafa Abrahamu: ndipo anazitcha maina monga maina omwe anazitcha atate wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa