Genesis 25:7 - Buku Lopatulika7 Masiku a zaka za moyo wake wa Abrahamu amene anakhala ndi moyo ndiwo zaka zana limodzi, kudza makumi asanu ndi limodzi, kudza khumi ndi zisanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Masiku a zaka za moyo wake wa Abrahamu amene anakhala ndi moyo ndiwo zaka zana limodzi, kudza makumi asanu ndi limodzi, kudza khumi ndi zisanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Abrahamu adakhala ndi moyo zaka 175. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Abrahamu anakhala ndi moyo zaka 175. Onani mutuwo |