Genesis 25:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo Abrahamu anamwalira, nafa mu ukalamba wake wabwino, nkhalamba ya zaka zambiri; natengedwa akhale ndi a mtundu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo Abrahamu anamwalira, nafa m'ukalamba wake wabwino, nkhalamba ya zaka zambiri; natengedwa akhale ndi a mtundu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Adamwalira ali nkhalamba yotheratu, atagonera zaka zochuluka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Abrahamu anamwalira atakalamba kwambiri ndipo anakakhala ndi anthu a mtundu wake. Onani mutuwo |