Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 24:64 - Buku Lopatulika

64 Ndipo Rebeka anatukula maso ake, ndipo pamene anaona Isaki anatsika pa ngamira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

64 Ndipo Rebeka anatukula maso ake, ndipo pamene anaona Isaki anatsika pa ngamira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

64 Tsono Rebeka ataona Isaki, adatsika pa ngamira yake ija,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

64 Rebeka nayenso anatukula maso naona Isake. Ndipo anatsika pa ngamira yake

Onani mutuwo Koperani




Genesis 24:64
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Isaki anatuluka kulingalira m'munda madzulo; ndipo anatukula maso ake, nayang'ana, taona, ngamira zinalinkudza.


Ndipo anati kwa mnyamata, Munthuyo ndani amene ayenda m'munda kukomana ndi ife? Mnyamatayo ndipo anati, Uyo ndi mbuyanga: chifukwa chake namwali anatenga chophimba chake nadziphimba.


Ndipo kunali, m'mene anamdzera, anamkangamiza mwamuna wake kuti apemphe atate wake ampatse munda; ndipo anatsika pabulu; pamenepo Kalebe ananena naye, Ufunanji?


Ndipo kunali, m'mene anamdzera, anamkakamiza mwamuna wake kuti apemphe atate wake ampatse munda; natsika pabulu wake; ndipo Kalebe ananena naye, Ufunanji?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa