Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 24:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo Abrahamu anati kwa iye, Chenjera iwe, usambwezerenso mwana wanga kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo Abrahamu anati kwa iye, Chenjera iwe, usambwezerenso mwana wanga kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Abrahamu adayankha kuti, “Usadzamperekeze kumeneko mwana wangayo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Abrahamu anati, “Uwonetsetse kuti usadzabwerere naye mwana wanga kumeneko.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 24:6
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anati kwa iye mnyamatayo, Kapena sadzafuna mkaziyo kunditsata ine ku dziko lino: kodi ndikambwezerenso mwana wanu ku dziko komwe mwachokera inu?


Ndipo ngati sadzafuna mkaziyo kukutsata iwe, udzakhala wosachimwa pa chilumbiro changachi: koma mwana wanga usambwezerenso kumeneko.


Khristu anatisandutsa mfulu, kuti tikhale mfulu; chifukwa chake chilimikani, musakodwenso ndi goli la ukapolo.


Koma ife si ndife a iwo akubwerera kulowa chitayiko; koma a iwo a chikhulupiriro cha ku chipulumutso cha moyo.


Ndi chikhulupiriro anakhala mlendo kudziko la lonjezano, losati lake, nakhalira m'mahema pamodzi ndi Isaki ndi Yakobo, olowa nyumba pamodzi ndi iye a lonjezano lomwelo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa