Genesis 24:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Abrahamu anati kwa iye, Chenjera iwe, usambwezerenso mwana wanga kumeneko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Abrahamu anati kwa iye, Chenjera iwe, usambwezerenso mwana wanga kumeneko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Abrahamu adayankha kuti, “Usadzamperekeze kumeneko mwana wangayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Abrahamu anati, “Uwonetsetse kuti usadzabwerere naye mwana wanga kumeneko. Onani mutuwo |