Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 24:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo anati kwa iye mnyamatayo, Kapena sadzafuna mkaziyo kunditsata ine ku dziko lino: kodi ndikambwezerenso mwana wanu ku dziko komwe mwachokera inu?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo anati kwa iye mnyamatayo, Kapena sadzafuna mkaziyo kunditsata ine ku dziko lino: kodi ndikambwezerenso mwana wanu ku dziko komwe mwachokera inu?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Koma wantchitoyo adafunsa kuti, “Nanga zidzatani mkaziyo akadzakana kubwera nane kuno? Kodi mwana wanuyo ndidzamperekeze ku dziko lanu kumene mudachokera?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Wantchito uja anafunsa kuti, “Nanga atakhala kuti mkaziyo sakufuna kubwera nane kuno? Kodi ine ndingadzatenge mwana wanu ndi kubwerera naye ku dziko kumene munachokera?”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 24:5
8 Mawu Ofanana  

Ndipo ndinati kwa mbuyanga, Kapena mkazi sadzanditsata ine.


Koma udzanke ku dziko langa, kwa abale anga, ndi kumtengera mwana wanga Isaki mkazi.


Ndipo anamuitana Rebeka nati kwa iye, Kodi udzanka pamodzi ndi munthuyo? Ndipo anati, Ndidzanka.


Ndipo Abrahamu anati kwa iye, Chenjera iwe, usambwezerenso mwana wanga kumeneko.


Usatchule dzina la Yehova Mulungu wako pachabe; chifukwa Yehova sadzamuyesa iye wosachimwa, amene atchula pachabe dzina lakelo.


Pakuti ukakana kuwalola amuke, ndi kuwagwira chigwiritsire,


Yense wochenjera amachita mwanzeru; koma wopusa aonetsa utsiru.


Ndipo udzalumbira, Pali Yehova m'zoonadi, m'chiweruziro, ndi m'chilungamo; ndipo mitundu ya anthu idzadzidalitsa mwa Iye, ndipo mwa Iye adzatamandira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa